Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 21:6-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Pakuti Ambuye atero kwa ine, Muka, ika mlonda anene cimene aciona;

7. ndipo pamene iye anaona khamu, amuna apakavalo awiri awiri, khamu la aburu, khamu la ngamila, iye adzamvetsera ndi khama mosamalitsa.

8. Ndipo iye anapfuulitsa ngati mkango, Ambuye inu, ine ndiimabe pamwamba pa nsanja nthawi ya usana, ndipo ndiikidwa mu ulonda wanga usiku wonse;

Werengani mutu wathunthu Yesaya 21