Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 19:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Katundu wa Aigupto.Taonani, Yehova wakwera pamwamba pa mtambo wothamanga, nadza ku Aigupto; ndi mafano a Aigupto adzagwedezeka pakufika kwace, ndi mtima wa Aigupto udzasungunuka pakati pace.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 19

Onani Yesaya 19:1 nkhani