Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 16:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma tsopano Yehova wanena, nati, Zisanapite zaka zitatu monga zaka za wolembedwa nchito, ulemerero wa Moabu udzakhala wonyozeka, ndi khamu lalikuru lace, ndi otsala adzakhala ang'ongong'ono ndi acabe.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 16

Onani Yesaya 16:14 nkhani