Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 15:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti kulira kwamveka kuzungulira malire a Moabu; kukuwa kwace kwafikira ku Eglaimu, ndi kukuwa kwace kwafikira ku Beerelimu.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 15

Onani Yesaya 15:8 nkhani