Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 15:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mtima wanga upfuula cifukwa ca Moabu: akuru ace athawira ku Zoari, ku Eglatiselisiya; pakuti pa cikweza ca Luhiti akwera alikulira, pakuti m'njira ya Horanaimu akweza mpfuu wa cionongeko.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 15

Onani Yesaya 15:5 nkhani