Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 10:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace padzaoneka, kuti pamene Ambuye atatha nchito yace yonse pa phiri la Ziyoni ndi pa Yerusalemu, ndidzalanga zipatso za mtima wolimba wa mfumu ya Asuri, ndi ulemerero wa maso ace okwezedwa.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 10

Onani Yesaya 10:12 nkhani