Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 9:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo apinda lilime lao ngati uta wao, liname; koma akula mphamvu m'dzikomo, koma si pacoonadi; pakuti alinkunkabe nacita zoipa, ndipo sandidziwa Ine, ati Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 9

Onani Yeremiya 9:3 nkhani