Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 52:32-34 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

32. nanena naye bwino, naika mpando wace upose mipando ya mafumu amene anali naye m'Babulo.

33. Ndipo anapindula zobvala zace za m'ndende, ndipo sanaleka kudya pamaso pace masiku onse a moyo wace.

34. Koma phoso lace mfumu ya ku Babulo sanaleka kumpatsa, phoso tsiku ndi tsiku gawo lace, mpaka tsiku la kufa kwace, masiku onse a moyo wace.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 52