Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 52:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo korona wamkuwa anali pamwamba pace; utari wace wa korona mmodzi unali wa mikono isanu, ndi made ndi makangaza pakorona pozungulira pace, onse amkuwa: nsanamira inzace yomwe inali nazo zonga zomwezi, ndi makangaza.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 52

Onani Yeremiya 52:22 nkhani