Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 52:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nsanamira ziwirizo, thawale limodzilo, ndi ng'ombe zamkuwa zinali pansi pa zoikapo, zimene mfumu Solomo anazipangira nyumba ya Yehova; mkuwa wa zipangizo zonsezi sanatha kuyesa kulemera kwace.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 52

Onani Yeremiya 52:20 nkhani