Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 51:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kwezani mbendera m'dziko, ombani lipenga mwa amitundu, konzerani amitundu amenyane naye, mummemezere maufumu a Ararati, Mini, ndi Asikenaza; muike nduna; amenyane naye; mukweretse akavalo ngati mandowa.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 51

Onani Yeremiya 51:27 nkhani