Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 51:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Muwakwezere mbendera makoma a Babulo, mulimbikitse ulonda, muike alonda, mupangiretu olalira, pakuti Yehova waganiziratu ndi kucita comwe ananena za okhala m'Babulo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 51

Onani Yeremiya 51:12 nkhani