Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 50:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Masiku omwewo, nthawi yomweyo, ati Yehova, ana a Israyeliadzadza, iwo ndi ana a Yuda; pamodzi adzayenda m'njira mwao alinkulira, nadzafuna Yehova Mulungu wao.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 50

Onani Yeremiya 50:4 nkhani