Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 46:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kwerani, inu akavalo; citani misala, inu magareta, aturuke amphamvu; Akusi ndi Aputi, ogwira cikopa; ndi Aludi, amene agwira ndi kukoka uta.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 46

Onani Yeremiya 46:9 nkhani