Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 46:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Za Aigupto: kunena za nkhondo ya Farao-neko mfumu ya Aigupto, imene inali pa nyanja ya Firate m'Karikemisi, imene anaikantha Nebukadirezara mfumu ya ku Babulo caka cacinai ca Yehoyakimu mwana wace wa Yosiya, mfumu ya Yuda.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 46

Onani Yeremiya 46:2 nkhani