Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 44:29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ici cidzakhala cizindikiro ca kwa inu, ati Yehova, cakuti Ine ndidzakulangani m'malo muno, kuti mudziwe kuti mau anga adzatsimikizidwatu akucitireni inu zoipa.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 44

Onani Yeremiya 44:29 nkhani