Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 44:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa mwafukiza, ndi cifukwa mwacimwira Yehova, osamvera mau a Yehova, osayenda m'cilamulo cace, ndi m'malemba ace, ndi m'mboni zace, cifukwa cace coipaci cakugwerani, monga lero lomwe.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 44

Onani Yeremiya 44:23 nkhani