Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 40:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yohanani mwana wa Kareya ananena kwa Gedaliya m'tseri, kuti, Ndimuketu, ndikaphe Ismayeli mwana wa Netaniya, anthu osadziwa; cifukwa canji adzakuphani inu, kuti Ayuda onse amene anakusonkhanira inu amwazike, ndi otsala a Yuda aonongeke?

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 40

Onani Yeremiya 40:15 nkhani