Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 40:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

pamenepo Ayuda onse anabwerera kufumira ku malo onse kumene anawaingitsirako, nafika ku dziko la Yuda, kwa Gedaliya, ku Mizipa, nasonkhanitsa vinyo ndi zipatso zamalimwe zambiri.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 40

Onani Yeremiya 40:12 nkhani