Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 4:28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cimeneco dziko lidzalira maliro, ndipo kumwamba kudzada; cifukwa ndanena, ndatsimikiza mtima, sindinatembenuka, sindidzabwerera pamenepo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 4

Onani Yeremiya 4:28 nkhani