Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 39:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Nebuzaradani kapitao wa alonda anatenga anthu otsalira m'mudzi, ndi othawa omwe, opandukira, ndi kumtsata ndi anthu otsalira nanka nao am'nsinga ku Babulo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 39

Onani Yeremiya 39:9 nkhani