Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 39:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma aumphawi a anthu, amene analibe kanthu, Nebuzaradani kapitao wa alonda anawasiya m'dziko la Yuda, nawapatsa mipesa ndi minda nthawi yomweyo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 39

Onani Yeremiya 39:10 nkhani