Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 38:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Taonani, akazi onse otsala m'nyumba ya mfumu ya Yuda adzaturutsidwa kunka kwa akuru a mfumu ya ku Babulo, ndipo akaziwo adzati, Oyanjana nanu anakunyengani, ndi kukuposani inu, mapazi anu amire m'thope, abwerera m'mbuyo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 38

Onani Yeremiya 38:22 nkhani