Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 38:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

koma ngati simudzaturukira kwa akuru a mfumu ya ku Babulo, mudziwu udzaperekedwa m'dzanja la Akasidi, ndipo udzatenthedwa ndi moto, ndipo simudzapulumuka m'manja mwao.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 38

Onani Yeremiya 38:18 nkhani