Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 37:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti ngakhale mukadakantha nkhondo yonse ya Akasidi akumenyana, nanu, ngakhale akadatsala olasidwa okha okha mwa iwo, koma iwowa akadauka yense m'hema wace ndi kutentha mudzi uwu ndi moto.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 37

Onani Yeremiya 37:10 nkhani