Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 36:29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo za Yehoyakimu mfumu ya Yuda uziti, Yehova atero: Iwe watentha mpukutu uwu, ndi kuti, Bwanji walemba m'menemo, kuti, Mfumu ya ku Babulo idzadzadi nidzaononga dziko ili, nidzatha m'menemo anthu ndi nvama?

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 36

Onani Yeremiya 36:29 nkhani