Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 35:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yeremiya anati kwa nyumba ya Arekabu, Atero Yehova wa makamu, Mulungu wa Israyeli: Cifukwa mwamvera lamulo la Yonadabu kholo lanu, ndi kusunga zonse anakulangizani inu, ndi kucita monga mwa zonse anakuuzani inu;

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 35

Onani Yeremiya 35:18 nkhani