Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 33:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

pamenepo pangano langa lidzasweka ndi Davide mtumiki wanga, kuti asakhale ndi mwana wamwamuna wakulamulira pa mpando wa ufumu wace; ndiponso ndi Alevi ansembe, atumiki anga.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 33

Onani Yeremiya 33:21 nkhani