Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 32:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Hanameli mwana wa mbale wa atate wanga anadza kwa ine m'bwalo la kaidi monga mwa mau a Yehova, nati kwa ine, Gulatu munda wanga, wa ku Anatoti, m'dziko la Benjamini; pakuti mphamvu yakulowa ndi yakuombola ndi yako; udzigulire wekha. Pamenepo ndinadziwa kuti awa ndi mau a Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 32

Onani Yeremiya 32:8 nkhani