Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 32:30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti ana a Israyeli ndi ana a Yuda anacita zoipa zokha zokha pamaso panga ciyambire ubwana wao, pakuti ana a Israyeli anandiputa Ine kokha kokha ndi nchito ya manja ao, ati Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 32

Onani Yeremiya 32:30 nkhani