Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 32:29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo Akasidi, olimbana ndi mudzi uwu, adzafika nadzayatsa mudziwu, nadzautentha, pamodzi ndi nyumba, zimene anafukizira Baala, pa macitidwe ao, ndi kutsanulirira milungu yina nsembe zothira, kuti autse mkwiyo wanga.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 32

Onani Yeremiya 32:29 nkhani