25. Ndipo Inu Yehova Mulungu mwati kwa ine, Udzigulire munda ndi ndalama, nuitane mboni; koma mudzi waperekedwa m'manja a Akasidi.
26. Ndipo anadza mau a Yehova kwa Yeremiya, kuti,
27. Taona, Ine ndine Yehova, Mulungu wa anthu lonse; kodi kuli kanthu kondilaka Ine?
28. Cifukwa cace Yehova atero: Taona, ndidzapereka mudziwu m'dzanja la Akasidi, m'dzanja la Nebukadirezara mfumu ya ku Babulo, ndipo iye adzaulanda,