Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 3:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo padzaoneka, pamene mudzakhala ambiri ndi kucuruka m'dzikomo masiku awo, ati Yehova, sadzatinso konse, Likasa la cipangano ca Yehova; silidzalowa m'mtima; sadzalikumbukira; sadzanka kukaliona, sadzacitanso konse.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 3

Onani Yeremiya 3:16 nkhani