Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 29:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yehova anakuyesa iwe wansembe m'malo mwa Yehoyada wansembe, kuti iwe ndi anzako mudzakhale akapitao m'nyumba ya Yehova, oyang'anira munthu yense wamisala, wodziyesa mneneri, kuti umuike iye m'zigologolo ndi m'gori.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 29

Onani Yeremiya 29:26 nkhani