Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 27:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ine ndinalenga dziko lapansi, anthu ndi nyama zokhala m'dzikomo, ndi mphamvu yanga yaikuru ndi mkono wanga wotambasuka; ndipo ndinapereka ilo kwa iye amene ayenera pamaso panga.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 27

Onani Yeremiya 27:5 nkhani