Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 27:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti sindinawatuma iwo, ati Yehova, koma anenera zonama m'dzina langa; kuti ndikupitikitseni inu, kuti mudzathedwe, inu, ndi aneneri amene anenera kwa inu.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 27

Onani Yeremiya 27:15 nkhani