Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 27:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndinanena kwa Zedekiya mfumu ya Yuda monga mau onse amenewa, kuti, Longani makosi anu m'gori la mfumu ya ku Babulo, ndi kumtumikira iye ndi anthu ace, ndipo mudzakhala ndi moyo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 27

Onani Yeremiya 27:12 nkhani