Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 26:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mika Mmorasi ananenera masiku a Hezekiya mfumu ya Yuda; ndipo iye ananena kwa anthu onse a Yuda, kuti, Yehova wa makamu atero: Ziyoni adzalimidwa ngati munda, Yerusalemu adzakhala miunda, ndi phiri la nyumba longa misanje ya nkhalango.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 26

Onani Yeremiya 26:18 nkhani