Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 25:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova watuma kwa inu atumiki ace onse ndiwo aneneri, pouka mamawa ndi kuwatuma; koma simunamvera, simunachera khutu lanu kuti mumve;

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 25

Onani Yeremiya 25:4 nkhani