Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 23:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Taonani, masiku alinkudza, ati Yehova, ndidzamuukitsira Davide Mphukira wolungama, ndipo Iye adzakhala Mfumu, adzacita mwanzeru, nadzacita ciweruzo ndi cilungamo m'dziko lino.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 23

Onani Yeremiya 23:5 nkhani