Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 23:34 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma za mneneri, ndi wansembe, ndi anthu, amene adzati, Katundu wa Yehova, ndidzamlanga munthuyo ndi nyumba yace.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 23

Onani Yeremiya 23:34 nkhani