Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 23:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace Yehova wa makamu atero za aneneri: Taonani, ndidzadyetsa iwo cowawa, ndidzamwetsa iwo madzi andulu; pakuti kwa aneneri a ku Yerusalemu kuipitsa kwaturukira kunka ku dziko lonse.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 23

Onani Yeremiya 23:15 nkhani