Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 20:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iwe, Pasuri, ndi onse okhala m'nyumba mwako mudzanka kundende; ndipo udzafika ku Babulo, ndi pamenepo udzafa, ndi pamenepo udzaikidwa, iwe, ndi mabwenzi ako onse, amene unawanenera mabodza.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 20

Onani Yeremiya 20:6 nkhani