Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 2:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, nati,

2. Pita nupfuule n'makutu a Yerusalemu, kuti, Yehova atero, Ndikumbukira za iwe kukoma mtima kwa ubwana wako, cikondi ca matomedwe ako; muja unanditsata m'cipululu m'dziko losabzya lamo.

3. Israyeli anali wopatulikira Yehova, zipatso zoundukula za zopindula zace; onse amene adzamudya iye adzayesedwa oparamula; coipa cidzawagwera, ati Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 2