Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 19:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa andisiya Ine, nayesa malo ano acilendo, nafukizira m'menemo milungu yina, imene sanaidziwa, iwowa, ndi makolo ao ndi mafumu a Yuda: nadzaza malo ano ndi mwazi wa osacimwa;

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 19

Onani Yeremiya 19:4 nkhani