Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 16:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo uziti kwa iwo, Cifukwa makolo anu anandisiya Ine, ati Yehova, natsata milungu yina, naitumikira, naigwadira, nandisiya Ine, osasunga cilamulo canga;

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 16

Onani Yeremiya 16:11 nkhani