Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 15:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndidzaika pa iwo mitundu inai, ati Yehova, lupanga lakupha, agaru akung'amba, mbalame za m'mlengalenga, ndi zirombo zapansi, zakulusa ndi kuononga.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 15

Onani Yeremiya 15:3 nkhani