Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 15:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace atero Yehova, Ukabwerera pamenepo ndidzakubwezanso, kuti uime pamaso panga; ndipo ukasiyanitsa ca mtengo wace ndi conyansa, udzakhala ngati m'kamwa mwanga; ndipo adzabwerera kwa iwe, koma sudzabwerera kwa iwo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 15

Onani Yeremiya 15:19 nkhani