Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 15:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kalanga ine, amai, pakuti mwandibala ine munthu wandeu, munthu wakutetana nalo dziko lonse lapansi! sindinakongoletsa paphindu, anthu sanandikongoletsa paphindu; koma iwo onse anditemberera.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 15

Onani Yeremiya 15:10 nkhani