Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 15:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova anati kwa ine, Ngakhale Mose ndi Samueli akadaima pamaso panga, koma mtima wanga sukadasamalira anthu awa; muwacotse iwo pamaso panga, aturuke.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 15

Onani Yeremiya 15:1 nkhani